19.02.2014 Views

KULIMA MU NJIRA YA MULUNGU - Farming God's Way

KULIMA MU NJIRA YA MULUNGU - Farming God's Way

KULIMA MU NJIRA YA MULUNGU - Farming God's Way

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

Kuomba mkota<br />

Ndi zinthu zodabwitsa kwambiri, chifukwa pamene tigwiritsa ntchito<br />

mfungulo zitatu zimenezi tidzapeza kuti tidzakhala ndi chimwemwe<br />

chochuluka chifukwa cha ntchito ya manja athu. Kumbukiraninso kuti<br />

mukafesa ndi chimwemwe, mudzatutanso ndi chimwemwe koma<br />

mukafesa ndi nkhope yokwiya, yong‟ung‟udza ndi kudandaula,<br />

mudzakololanso ndikung‟ung‟udza.<br />

<br />

2 Akorinto 9:7 “Munthu wina aliyense achite monga<br />

waganizira mumtima mwake: osati mokakamiza ndi<br />

mwakusafuna: pakuti Mulungu amakonda opereka<br />

mwachimwemwe.”<br />

Kukhumba kwathu kuti tikayang‟anire bwino, komanso kuti tikapeze<br />

phindu lopitirira, ndi chinthu chachiwiri mumayendedwe oyenera<br />

kutchedwa ana ake. Tikuyenera kuchita china chiri chonse chimene<br />

timapanga ngati tikupangira Yehova, ndi zipatso zonse za Mzimu<br />

Woyera zikuoneka monga umboni wa ntchito imene Mulungu<br />

wachita m‟moyo wathu.<br />

31

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!