KULIMA MU NJIRA YA MULUNGU - Farming God's Way
KULIMA MU NJIRA YA MULUNGU - Farming God's Way
KULIMA MU NJIRA YA MULUNGU - Farming God's Way
You also want an ePaper? Increase the reach of your titles
YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.
Kuomba mkota<br />
Ndi zinthu zodabwitsa kwambiri, chifukwa pamene tigwiritsa ntchito<br />
mfungulo zitatu zimenezi tidzapeza kuti tidzakhala ndi chimwemwe<br />
chochuluka chifukwa cha ntchito ya manja athu. Kumbukiraninso kuti<br />
mukafesa ndi chimwemwe, mudzatutanso ndi chimwemwe koma<br />
mukafesa ndi nkhope yokwiya, yong‟ung‟udza ndi kudandaula,<br />
mudzakololanso ndikung‟ung‟udza.<br />
<br />
2 Akorinto 9:7 “Munthu wina aliyense achite monga<br />
waganizira mumtima mwake: osati mokakamiza ndi<br />
mwakusafuna: pakuti Mulungu amakonda opereka<br />
mwachimwemwe.”<br />
Kukhumba kwathu kuti tikayang‟anire bwino, komanso kuti tikapeze<br />
phindu lopitirira, ndi chinthu chachiwiri mumayendedwe oyenera<br />
kutchedwa ana ake. Tikuyenera kuchita china chiri chonse chimene<br />
timapanga ngati tikupangira Yehova, ndi zipatso zonse za Mzimu<br />
Woyera zikuoneka monga umboni wa ntchito imene Mulungu<br />
wachita m‟moyo wathu.<br />
31