10.03.2017 Views

Miyambi ya Patsokwe by Bonwell Rodgers

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

apa anthu angakuphe,” koma Kalikongwe<br />

sanamvere. Anzakewo atachoka,<br />

kunabweradi anthu ndipo atamupeza<br />

anamupha n’kukamudyera nsima.<br />

Adatha mphika ndi “n’talawa.”<br />

-Kukomedwa ndi chinthu kumapangitsa kuti<br />

uzolowere kenako umatha kupalamula.<br />

Adera amakoma pod<strong>ya</strong> nawo.<br />

-Anthu adera amakonda munthu akakhala<br />

pabwino koma zikamuvuta kapena<br />

akasauka, amamuthawa. Achibale ake okha<br />

ndi amene amamusamalabe.<br />

Adye zabwino anad<strong>ya</strong> zowawa.<br />

-Mwambiwu umachenjeza munthu amene<br />

amafuna atapeza zabwino zonse nthawi<br />

imodzi. Akapanda kusamala amatha<br />

kukumana ndi mavuto. Choncho, zabwino<br />

zimabwera pang’onopang’ono, munthu<br />

amangofunika kudikira kuti nthawi <strong>ya</strong>ke<br />

<strong>Mi<strong>ya</strong>mbi</strong> <strong>ya</strong> <strong>Patsokwe</strong><br />

5

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!