Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
STRATEGIC IMPACT - SUKULU YOCHULUTSA AZITSOGOLELI<br />
PHUNZILO 6 - UBYALA MIPINGO<br />
“MFUNDO 2: PEMPHERO”<br />
Pamene muyamba ukumana, gawanikani mʼmagulu ya anthu ANAI pagulu limodzi<br />
pampindi zokwanila ngati makumi yatatu mwina mwache mochepekela.<br />
Muphephererani wina ndi mzache ndipo mufunsane mafunso ya ungwilo. Pambuyo<br />
pache nkhalaninso mʼmagulu anu ndiku werenga phunzilo ili ndiku ponyapo<br />
ndemanga.<br />
WERENGANI: Machitidwe 2:42, Akolose 4:2-4, Aroma12:12, 1 John 5:14-15, &<br />
" " " Luka 10:2-3<br />
! Mukayamba usintha maganizo yanu ku chokela ku maganizo yo manga Ufumu<br />
wanu (zimango za ma chalichi/ma pologilamu/ndalama zambiri,ndi zina zache.) kuti<br />
yakhali ma ganizo yo manga Ufumu wa Mulungu, muzaona zazikulu zomwe Mulungu<br />
aku konzelani. Nchito yomwe Mulungu anati itanila ndiku pereka uthenga kwa anthu<br />
wosowa” (Matteo 28:18-20, Machitidwe 1:8). Uphunzitsa amitundu ndi nchito ya<br />
Mzimu Woyera (Yohane 6:65, 3:27). Utumiki wo pereka uthenga kwa anthu amitundu<br />
ndi nchito ya mkristu aliyense ali padziko lapansi. kulibe munthu kapena gulu la anthu<br />
omwe anga kwanise upereka uthenga ku mbali zonse za padziko lapansi pa iwo okha”<br />
! Mulungu ati lamulila kuti ise tigwile nchito yo pambana pamvu zathu za umunthu.<br />
Chakhala ngati chintu chapa fupi kwa ise kuti tiiwale nchito yo pereka ulaliki kwa<br />
osowa. Yesu anati, “Ulamulilo wapadziko la kumwamba ndi dziko lapansi la patsidwa<br />
kwa ine.” Analankhulanso kuti, “koma inu muzalandila mpamvu pamene Mzimu Oyera<br />
adzadza pa inu.” Ngati mulungu atilamula, tikhulupirira kuti adza tipasa pamvu kenaka<br />
zonse zofunikila kuti ifeyo tikwanilitse zomwe atilamulila – timupemphe Mulungu mwa<br />
chi khulupiriro! Mu buku la 1Yohane 5:14-15, malemba yakuti, “And this is the<br />
confidence that we have toward him, that if we ask anything according to his will he<br />
hears us. And if we know that he hears us in whatever we ask, we know that we have<br />
the requests that we have asked of him.” Ndikufunsani inuyo: kodi chikwanilitso cho<br />
pereka uthenga kwa amitundu ndi chifunilo cha Mulungu? INDE ! INDE!! INDE!!!<br />
Kodi Ambuye Yesu ali ndi mpamvu kuti akwanilitse nchito yo pereka ulaliki kwa<br />
amitundu ? INDE! INDE!! INDE!!! Kodi chimenechi azachikwanilitsa bwanji?<br />
Kupyolela mwa mpanvu Zache ndi zi nchito zathu!<br />
NDEMANGA/MAFUNSO: Nichifukwa ninji timadalila mpamvu zathu, mpaso zathu kenaka<br />
" ukatswili wathu kuti tikwanilise nchito yomwe Mulungu anatipasa?<br />
! 30