21.06.2013 Views

Tsiku 1 - strategic impact

Tsiku 1 - strategic impact

Tsiku 1 - strategic impact

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

STRATEGIC IMPACT - SUKULU YOCHULUTSA AZITSOGOLELI<br />

PHUNZILO 10 - UTUKULA ZA UMOYO<br />

“CHITSANZO CHAPEPHERO - PEMPERO YA AMBUYE”<br />

Pamene muyamba ukumana, gawanikani mʼmagulu ya anthu ANAI pagulu limodzi<br />

pampindi zokwanila ngati makumi yatatu mwina mwache mochepekela.<br />

Muphephererani wina ndi mzache ndipo mufunsane mafunso ya ungwilo. Pambuyo<br />

pache nkhalaninso mʼmagulu anu ndiku werenga phunzilo ili ndiku ponyapo<br />

ndemanga.<br />

WELENGANI: Mateyo 6:5-15<br />

! Pemphero ndiye njila yakuyanjanitsa inu ndi Mulungu. Ngati akristo, Mulungu<br />

anati pasa ndanga kuti tidze kwa iye, Mlengi wa zonse ndiponso Mfumu wa zonse.<br />

Pakuti malemba yati sonyeza malamulo momwe tinga pempherere, ndiye kuti kulinso<br />

njila yo vomekezedwa ndi yo savomekezedwa po bwera pamaso pa Mulungu. Ambuye<br />

yesu anati phunzitsa momwe tiyenela kupepherera. Mu buku la Mateo 6:5-8 Ambuye<br />

Yesu anatipasa malamulu yomwe tiyenela kusata tisane pemphere, mu Mateo 6:9-13.<br />

Ambuyeanatipasa pemphero mwachitsanzo. Mu Mateo 6:14-15 anati pansanso ku<br />

unikilidwa kut pemphero ifunikila ku khali ndi choonadi.<br />

ZOFUNIKILA TISANAYAMBE UPEMPHELA:<br />

Mateo 6:5-6 Ilankhula kuti tisama phemphera ngati “achinyengo”. Simupemphera<br />

kuti muonekele ku anthu. Simupephera kuti mukodweretse anthu ndi mau apemphero<br />

lanu. Anthu ambili agwa mu msapha umeneyu kuti akaonekele ali kupemphera pagulu<br />

la anthu kuti anthu atione ngati auzimu kapena akatswili amapephero. Mwa choonadi<br />

mtima wathu ukufube ulemelelo wathu osati wa Mulungu. Chimenechi chitsonyeza kuti<br />

ise sindise Auzimua!<br />

! Popephera ndicho funikila kuti mulowe mchipinda muli mwekha. Mulungu ama<br />

timva ngakhale pomwe tili mʼmalo achisinsi. Kodi chimenechi chitanthauza kuti sitinga<br />

pemphere pa gulu ya anthu? Kodi chilibwanji chimenechi? Pemphero ya chitsanzo pa<br />

ndime 7-13 ina perekedwa pakati pa iwo omwe Ambuye Yesu anali kuphunzitsa. Kuli<br />

zitsanzo zambili mchipangano chatsopano pomwe mapemphero yana perekedwa pa<br />

gulu la anthu. Sikuchimwa ai ngati tiku pemphera pa gulu la anthu, koma ndi chimo<br />

ngati tiku pemphera ngati achinyengo- kuti tionekele ku anthu. Ngati simukwanilisa<br />

upemphera pagulu popanda kugwa mumuyeso uwu ndi bwino kupita kwa mwekha<br />

kuka pemphera.<br />

NDEMANGA/MAFUNSO: Kodi tinga pewe bwanji chikhalidwe chopemphera kuti tionekele<br />

" ku anthu?<br />

! 44

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!