You also want an ePaper? Increase the reach of your titles
YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.
STRATEGIC IMPACT - SUKULU YOCHULUTSA AZITSOGOLELI<br />
PHUNZILO 10 - UTUKULA ZA UMOYO<br />
“CHITSANZO CHAPEPHERO - PEMPERO YA AMBUYE”<br />
Pamene muyamba ukumana, gawanikani mʼmagulu ya anthu ANAI pagulu limodzi<br />
pampindi zokwanila ngati makumi yatatu mwina mwache mochepekela.<br />
Muphephererani wina ndi mzache ndipo mufunsane mafunso ya ungwilo. Pambuyo<br />
pache nkhalaninso mʼmagulu anu ndiku werenga phunzilo ili ndiku ponyapo<br />
ndemanga.<br />
WELENGANI: Mateyo 6:5-15<br />
! Pemphero ndiye njila yakuyanjanitsa inu ndi Mulungu. Ngati akristo, Mulungu<br />
anati pasa ndanga kuti tidze kwa iye, Mlengi wa zonse ndiponso Mfumu wa zonse.<br />
Pakuti malemba yati sonyeza malamulo momwe tinga pempherere, ndiye kuti kulinso<br />
njila yo vomekezedwa ndi yo savomekezedwa po bwera pamaso pa Mulungu. Ambuye<br />
yesu anati phunzitsa momwe tiyenela kupepherera. Mu buku la Mateo 6:5-8 Ambuye<br />
Yesu anatipasa malamulu yomwe tiyenela kusata tisane pemphere, mu Mateo 6:9-13.<br />
Ambuyeanatipasa pemphero mwachitsanzo. Mu Mateo 6:14-15 anati pansanso ku<br />
unikilidwa kut pemphero ifunikila ku khali ndi choonadi.<br />
ZOFUNIKILA TISANAYAMBE UPEMPHELA:<br />
Mateo 6:5-6 Ilankhula kuti tisama phemphera ngati “achinyengo”. Simupemphera<br />
kuti muonekele ku anthu. Simupephera kuti mukodweretse anthu ndi mau apemphero<br />
lanu. Anthu ambili agwa mu msapha umeneyu kuti akaonekele ali kupemphera pagulu<br />
la anthu kuti anthu atione ngati auzimu kapena akatswili amapephero. Mwa choonadi<br />
mtima wathu ukufube ulemelelo wathu osati wa Mulungu. Chimenechi chitsonyeza kuti<br />
ise sindise Auzimua!<br />
! Popephera ndicho funikila kuti mulowe mchipinda muli mwekha. Mulungu ama<br />
timva ngakhale pomwe tili mʼmalo achisinsi. Kodi chimenechi chitanthauza kuti sitinga<br />
pemphere pa gulu ya anthu? Kodi chilibwanji chimenechi? Pemphero ya chitsanzo pa<br />
ndime 7-13 ina perekedwa pakati pa iwo omwe Ambuye Yesu anali kuphunzitsa. Kuli<br />
zitsanzo zambili mchipangano chatsopano pomwe mapemphero yana perekedwa pa<br />
gulu la anthu. Sikuchimwa ai ngati tiku pemphera pa gulu la anthu, koma ndi chimo<br />
ngati tiku pemphera ngati achinyengo- kuti tionekele ku anthu. Ngati simukwanilisa<br />
upemphera pagulu popanda kugwa mumuyeso uwu ndi bwino kupita kwa mwekha<br />
kuka pemphera.<br />
NDEMANGA/MAFUNSO: Kodi tinga pewe bwanji chikhalidwe chopemphera kuti tionekele<br />
" ku anthu?<br />
! 44