21.06.2013 Views

Tsiku 1 - strategic impact

Tsiku 1 - strategic impact

Tsiku 1 - strategic impact

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

STRATEGIC IMPACT - SUKULU YOCHULUTSA AZITSOGOLELI<br />

PHUNZILO 8 - UTUKULA UTSOGOLELI<br />

“CHIKHALIDWE: ZOFUNIKILA PA UMOYO WA MTOGOLELI”<br />

Pamene muyamba ukumana, gawanikani mʼmagulu ya anthu ANAI pagulu limodzi<br />

pampindi zokwanila ngati makumi yatatu mwina mwache mochepekela.<br />

Muphephererani wina ndi mzache ndipo mufunsane mafunso ya ungwilo. Pambuyo<br />

pache nkhalaninso mʼmagulu anu ndiku werenga phunzilo ili ndiku ponyapo<br />

ndemanga.<br />

! Mtsogoleli anga khale ndi maso mpenya yayakhulu ndi mchango koma kuli<br />

chikhalidwe chichikulu chomwe afunika ukhala nacho, afunika ukhala okhulupilika.<br />

Chilibe kanthu ngakhali kuti mstogoleli ali ndi mchangu ndi maso mpenya yampamvu<br />

koma ngati sakhulupirika zonsezi zili mwachabe, anthu sadzalondola mtsogoleli otele!<br />

Ngati mstogoleli mataya chikhulupililo cha anthu, anthu saza mulondola. Choncho<br />

ngati mtsogoleli wa umulungu akufuna utakasa ina ndiku kwanilisa maso mpenya yaya<br />

kulu ndibwino kuti akhale ndi CHIKHALIDWE chabwino.<br />

! Kodi chikhalidwe ndi chiani? Chikhalidwe ndi ku khulupirika komwe kumabwera<br />

kamba ka kusonyeza.<br />

! Modzi wa atsogoleli ampamvu mu Baibulo ndi Mfumu Davide. Nichifukwa ninji<br />

anali woposa? Masalimo 78:72 itipasa yankho. “And ndipo Davide ana tsogolela ndi<br />

mtima wa mtima wa Ungwilo ndi manja ya luso.” Davide sana tsogolele chabe ndi luso<br />

komabe anasonyeza ukhulupirika. Ukhulupirika ndiku nkhala okwana ndipo<br />

osagawikana.ʼ Ndiku khali ukhulupirika ndipo opanda chinyengo kapena<br />

kunyalanyaza. Munthu okhulupilika ndi munthu amene ali oyela mtima. Sasintha<br />

pomwe ali okha ndi pmwe ali pakati ka anthu. Ndi okhulupirika ndiponso odalilika.<br />

Achita zomwe alankhula ndipo asonga mau yao. Munthu wa ungwilo kapena<br />

okhulupilika siuja munthu wamene alibe chilema kapena banga kapena wamene<br />

sachimwa ai. Ichi sichotheka ai. Komabe ndi munthu wamene avomeleza ngati alakwa<br />

ndi ku ululila machimo yake. Chifukwa chakuti asonyeza ukhulupilika nthawi zonse,<br />

ena aphunzila ndi ku dalila iwo.<br />

NDEMANGA/MAFUNSO:<br />

1. Nichifukwa ninji chikhalidwe kapena ungwilo chili chofunika kwa atsogoleli a<br />

umulungu?<br />

2. Nichifukwa ninji chikhalidwe chosa yeluzika ndi cho optsa osogoleli wa chikristu?<br />

3. Ndi njila zotani zomwe mtsogoleli wa chi kristu kusonyeza kuti ndi okhulupilikay?<br />

! 38

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!