21.06.2013 Views

Tsiku 1 - strategic impact

Tsiku 1 - strategic impact

Tsiku 1 - strategic impact

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

STRATEGIC IMPACT - SUKULU YOCHULUTSA AZITSOGOLELI<br />

PHUNZILO 9 - UBYALA MIPINGO<br />

“MFUNDO 3 & 4: SONKHANITSANI NDI KUPHUNZITSA OPANGA OPHUNZILA”<br />

Pamene muyamba ukumana, gawanikani mʼmagulu ya anthu ANAI pagulu limodzi<br />

pampindi zokwanila ngati makumi yatatu mwina mwache mochepekela.<br />

Muphephererani wina ndi mzache ndipo mufunsane mafunso ya ungwilo. Pambuyo<br />

pache nkhalaninso mʼmagulu anu ndiku werenga phunzilo ili ndiku ponyapo<br />

ndemanga.<br />

Mphunzitsani GULU, osati chabe “Mtsogoleli”<br />

! Mtsogoleli wachi kristu aliyese ali kuchita zazikhulu padziko lapansi, sachita<br />

zimenezi payekha ai. Yesu Kristu anali ndi ʻguluʼ la atumwi khumi ndi awiri amene iye<br />

ana phunzitsa ndi ku wutuma padziko lapansi. Mtumwi Paulo anali ndi gulu lakenso.<br />

Sanachite utumiki payekha. Ngati mukufuna ukwanilisa ku itanidwa kwa Mulungu pa<br />

umoyo wanu ndi bwino kuti mumange gulu lo chulukitsa Ophunzila amene ali<br />

ozipereka ku utumiki wa mau pa dziko lapansi. Lingalilani izi po sonkhanitsa ndi<br />

kuphunzitsa gulu lanu;<br />

1. Zindikilani maso mpenya ya Mulungu pa umoyo wanu.<br />

! Malemba yakuti pa nkhani ya Davide, “pamene Davide ana tumikila lingo la<br />

! Mulungu kwa mʼbadwe wake kulingani ndi chifunila cha Mulungu, ana<br />

! mwalila.” [Acts 13:36]<br />

! Kulibe mau yabwino yopambana aya kuti yakalankhulidwe pa imoyo wathu - kuti<br />

! tina kwanilitsa chifunilo cha Mulungu mu ʻbadwo wathu! Inu simunalengedwe ai.<br />

! Sichangozi kuti inu ndinu mwana wa Mulungu pa nthawi ino ndi pamalo pomwe<br />

! mukukhala. Mulungu ali ndi lingo lalikhula pa umoyo wanu. Ana ku itanani kuti<br />

! muchite chifunilo chache!<br />

NDEMANGA/MAFUNSO: Nichifukwa ninji Mulungu ana ku ikani padziko lapansi pa<br />

" nthawi ino?<br />

" Kodi ku itana kwa Mulungu pa umoyo wanu mukukudziwa?<br />

" Kodi chomwe mukufunisisa pa umoyo wanu chopambana zonse ndi chiani?<br />

2. Mupepheni Mulungu kuti abweletse Anthu okuthandizani kuti mukwanilitse<br />

Maso Mpenya yanu.<br />

! Mako 3:14 itisonyeza momwe Yesu anasankhila gulu yake kuti akwanilitse lingo<br />

! lache padziko lapansi.“ndipo anasakha khumi ndi awiri kuti akhale nao , andi<br />

! kuwa tuma kuti akalalike uthenga wa Mulungu.”<br />

! 40

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!